Ahebri 3:7 - Buku Lopatulika7 Momwemo, monga anena Mzimu Woyera, Lero ngati mudzamva mau ake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Momwemo, monga anena Mzimu Woyera, Lero ngati mudzamva mau ake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake tsono, monga Mzimu Woyera akunenera, “Lero lino mukamva mau a Mulungu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsono monga Mzimu Woyera akuti, “Lero mukamva mawu ake, Onani mutuwo |