Ahebri 3:19 - Buku Lopatulika19 Si awo kodi osamverawo? Ndipo tiona kuti sanathe kulowa chifukwa cha kusakhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Si awo kodi osamverawo? Ndipo tiona kuti sanakhoza kulowa chifukwa cha kusakhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Motero tikuwona kuti anthuwo sadathe kuloŵa, chifukwa cha kusakhulupirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Tsono ife tikuona kuti sanalowe chifukwa cha kusakhulupirika kwawo. Onani mutuwo |