Ahebri 3:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo adawalumbirira ayani kuti asalowe mpumulo wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo adawalumbirira ayani kuti asalowe mpumulo wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nanga Mulungu ankanena za yani pamene adaati, “Ndikulumbira kuti ameneŵa sadzaloŵa konse mu mpumulo umene ndidaŵakonzera?” Pajatu ankanena za anthu amene adaamuukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nanga Mulungu ankanena za ndani kuti sadzalowa mu mpumulo wake? Pajatu ankanena za anthu amene sanamvere aja. Onani mutuwo |