Ahebri 3:17 - Buku Lopatulika17 Koma anakwiya ndi ayani zaka makumi anai? Kodi si ndi awo adachimwawo, amene matupi ao adagwa m'chipululu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma anakwiya ndi ayani zaka makumi anai? Kodi si ndi awo adachimwawo, amene matupi ao adagwa m'chipululu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Nanga amene Mulungu adaaŵakwiyira zaka makumi anai, ndani? Ndi anthu amene adaachimwa aja, mitembo yao nkutsalira m'chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Nanga amene Mulungu anawakwiyira zaka makumi anayi anali ndani? Kodi si anthu amene anachimwa, amene mitembo yawo inatsala mʼchipululu muja? Onani mutuwo |