Ahebri 3:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti ndi ayani, pakumva, anapsetsa mtima? Kodi si onse aja adatuluka mu Ejipito ndi Mose? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti ndi ayani, pakumva, anapsetsa mtima? Kodi si onse aja adatuluka m'Ejipito ndi Mose? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nanga amene adaamva mau ake a Mulungu namuukira, ndani? Ndi onse aja amene Mose adaaŵatsogolera nkuŵatulutsa m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Nanga amene anamva ndi kuwukira anali ndani? Kodi si onse amene Mose anawatulutsa mu Igupto? Onani mutuwo |