Ahebri 3:15 - Buku Lopatulika15 umo anenamo, Lero ngati mudzamva mau ake, musaumitse mitima yanu, monga pa kupsetsa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 umo anenamo, Lero ngati mudzamva mau ake, musaumitse mitima yanu, monga pa kupsetsa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Paja Malembo akuti, “Lero lino mukamva mau a Mulungu, musaumitse mitima yanu monga muja zidaachitikira poukira Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Monga kunanenedwa kuti, “Lero ngati mumva mawu ake, musawumitse mitima yanu ngati momwe munachitira pamene munawukira.” Onani mutuwo |