Ahebri 3:14 - Buku Lopatulika14 pakuti takhala ife olandirana ndi Khristu, ngatitu tigwiritsa chiyambi cha kutama kwathu kuchigwira kufikira chitsiriziro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 pakuti takhala ife olandirana ndi Khristu, ngatitu tigwiritsa chiyambi cha kutama kwathu kuchigwira kufikira chitsiriziro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Paja timasanduka anzake a Khristu, malinga tikasunga kwenikweni mpaka potsiriza kulimba mtima kumene tinali nako poyamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti timakhala anzake a Khristu, ngati tigwiritsitsa mpaka potsiriza chitsimikizo chimene tinali nacho pachiyambi. Onani mutuwo |