Ahebri 2:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti ndithu salandira angelo, koma alandira mbeu ya Abrahamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti ndithu salandira angelo, koma alandira mbeu ya Abrahamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Paja nchodziŵikiratu kuti sadatekeseke ndi angelo ai koma ndi zidzukulu za Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pakuti tikudziwanso kuti sathandiza angelo, koma zidzukulu za Abrahamu. Onani mutuwo |