Ahebri 2:15 - Buku Lopatulika15 nakamasule iwo onse amene, chifukwa cha kuopa imfa, m'moyo wao wonse adamangidwa ukapolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 nakamasule iwo onse amene, chifukwa cha kuopa imfa, m'moyo wao wonse adamangidwa ukapolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pakutero adafunanso kuti aŵamasule amene pa moyo wao wonse anali ngati akapolo chifukwa choopa imfa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pakuti ndi njira yokhayi imene Iye angamasule amene pa moyo wawo wonse anali ngati akapolo chifukwa choopa imfa. Onani mutuwo |