Ahebri 13:23 - Buku Lopatulika23 Zindikirani kuti mbale wathu Timoteo wamasulidwa; pamodzi ndi iye, ngati akudza msanga, ndidzakuonani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Zindikirani kuti mbale wathu Timoteo wamasulidwa; pamodzi ndi iye, ngati akudza msanga, ndidzakuonani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndikufuna kuti mudziŵe kuti Timoteo, mbale wathu, amtulutsa m'ndende. Akafika msanga, ndidzabwera naye kwanuko podzakuwonani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ine ndikufuna kuti inu mudziwe kuti mʼbale wathu Timoteyo wamasulidwa. Ngati iye angafike msanga ndibwera naye kudzakuonani. Onani mutuwo |