Ahebri 13:24 - Buku Lopatulika24 Perekani moni kwa atsogoleri anu onse, ndi oyera mtima onse. Akupatsani moni iwo a ku Italiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Perekani moni kwa atsogoleri anu onse, ndi oyera mtima onse. Akupatsani moni iwo a ku Italiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mutiperekereko moni kwa atsogoleri anu onse, ndi kwa anthu onse a Mulungu. Abale a ku Italiya akuti moni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mupereke moni kwa atsogoleri anu onse ndiponso kwa anthu onse a Mulungu. Abale ochokera ku Italiya akupereka moni. Onani mutuwo |