Ahebri 13:22 - Buku Lopatulika22 Koma ndidandaulira inu, abale, lolani mau a chidandauliro; pakutinso ndalembera inu mwachidule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma ndidandaulira inu, abale, lolani mau a chidandauliro; pakutinso ndalembera inu mwachidule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndikukupemphani, inu abale anga, kuti muŵalandire bwino mau okulimbitsani mtimaŵa, pakuti ndangokulemberani mwachidule. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndikukupemphani abale kuti mulandire mawu anga achilimbikitso, pakuti ndakulemberani mwachidule. Onani mutuwo |