Ahebri 13:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake titulukire kwa Iye kunja kwa tsasa osenza tonzo lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake titulukire kwa Iye kunja kwa tsasa osenza tonzo lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Tiyeni tsono tipite kwa Iye kunja kwa misasa kuti tikanyozekere naye limodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Tiyeni tsono, tipite kwa iye kunja kwa msasa, titasenza chitonzo chake. Onani mutuwo |