Ahebri 13:12 - Buku Lopatulika12 Mwa ichi Yesunso, kuti akayeretse anthuwo mwa mwazi wa Iye yekha, adamva chowawa kunja kwa chipata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mwa ichi Yesunso, kuti akayeretse anthuwo mwa mwazi wa Iye yekha, adamva chowawa kunja kwa chipata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chifukwa cha chimenechi, Yesu nayenso adafera kunja kwa mzinda, kuti pakutero ayeretse anthu ndi magazi ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Nʼchifukwa chakenso Yesu anafera kunja kwa mzinda kuti ayeretse anthu ake kudzera mʼmagazi ake. Onani mutuwo |