Ahebri 13:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti pano tilibe mzinda wokhalitsa, komatu tifunafuna ulinkudzawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti pano tilibe mudzi wokhalitsa, komatu tifunafuna ulinkudzawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Paja ife tilibe mzinda wokhazikika pansi pano, tikufunafuna wina umene ulikudza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti ife tilibe mzinda wokhazikika koma tikudikira mzinda umene ukubwera. Onani mutuwo |