Ahebri 12:7 - Buku Lopatulika7 Mukapirira kufikira kulangidwa Mulungu achitira inu monga ngati ana; pakuti mwana wanji amene atate wake wosamlanga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Mukapirira kufikira kulangidwa Mulungu achitira inu monga ngati ana; pakuti mwana wanji amene atate wake wosamlanga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Muzipirira masautso kuti muphunzirepo makhalidwe oyenera. Mulungu amakutengani ngati ana ake m'zochita zake zonse. Kodi nkale lonse analipo mwana amene bambo wake sadamlange? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene mukupirira masautso monga chilango, Mulungu achitira inu monga ana ake. Kodi ndi mwana wotani amene abambo ake samulanga? Onani mutuwo |