Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 12:8 - Buku Lopatulika

8 Koma ngati mukhala opanda chilango, chimene onse adalawako, pamenepo muli am'thengo, si ana ai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Koma ngati mukhala opanda chilango, chimene onse adalawako, pamenepo muli am'thengo, si ana ai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ngati Mulungu sakulangani inuyo, monga amachitira ndi ana ake onse, ndiye kuti sindinu ana enieni, koma am'chigololo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ngati inu simulangidwa, komatu aliyense amalangidwa, ndiye kuti sindinu ana enieni koma amʼchigololo.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 12:8
5 Mawu Ofanana  

Indedi Mulungu achitira Israele zabwino, iwo a mtima wa mbee.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


pakuti iye amene Ambuye amkonda amlanga, nakwapula mwana aliyense amlandira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa