Ahebri 11:25 - Buku Lopatulika25 nasankhula kuchitidwa zoipa pamodzi ndi anthu a Mulungu, kosati kukhala nazo zokondweretsa za zoipa nthawi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 nasankhula kuchitidwa zoipa pamodzi ndi anthu a Mulungu, kosati kukhala nazo zokondweretsa za zoipa nthawi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Iye adasankha kuzunzikira nawo limodzi ana a Mulungu, koposa kukondwerera zosangalatsa za uchimo kanthaŵi pang'ono. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iye anasankha kuzunzika nawo limodzi anthu a Mulungu kuposa kusangalala ndi zokondweretsa za uchimo kwa nthawi yochepa. Onani mutuwo |