Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 11:24 - Buku Lopatulika

24 Ndi chikhulupiriro Mose, atakula msinkhu, anakana kutchedwa mwana wake wa mwana wamkazi wa Farao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndi chikhulupiriro Mose, atakula msinkhu, anakana kutchedwa mwana wake wa mwana wamkazi wa Farao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Pokhala ndi chikhulupiriro, Mose atakula adakana kutchedwa mdzukulu wa Farao, mfumu ya ku Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Ndi chikhulupiriro Mose atakula, anakana kutchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:24
2 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa