Ahebri 11:26 - Buku Lopatulika26 nawerenga tonzo la Khristu chuma choposa zolemera za Aejipito; pakuti anapenyerera chobwezera cha mphotho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 nawerenga tonzo la Khristu chuma choposa zolemera za Aejipito; pakuti anapenyerera chobwezera cha mphotho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Adaaona kuti kuzunzika chifukwa cha Wodzozedwa wa Mulungu kunali chuma chachikulu koposa chuma chonse cha ku Ejipito, pakuti maso ake anali ndithu pa mphotho yakutsogolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Anaona kuti kuzunzika chifukwa cha Khristu kunali kwa mtengowapatali kuposa chuma cha ku Igupto, chifukwa amaona mphotho ya mʼtsogolo. Onani mutuwo |