Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 11:21 - Buku Lopatulika

21 Ndi chikhulupiriro Yakobo, poti alinkufa, anadalitsa yense wa ana a Yosefe; napembedza potsamira pamutu wa ndodo yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndi chikhulupiriro Yakobo, poti alinkufa, anadalitsa yense wa ana a Yosefe; napembedza potsamira pa mutu wa ndodo yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pokhala ndi chikhulupiriro, Yakobe pakufa, adadalitsa ana a Yosefe mmodzimmodzi. Pochita zimenezi anali atayedzamira pa ndodo yake, akupembedza Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ndi chikhulupiriro, pamene Yakobo ankamwalira anadalitsa ana awiri a Yosefe, ndipo anapembedza Mulungu atatsamira ndodo yake.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:21
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Undilumbirire ine; namlumbirira iye. Ndipo Israele anawerama kumutu kwa kama.


Ndipo panali zitapita izi, anthu anati kwa Yosefe, Taonani, atate wanu wadwala: ndipo iye anatenga ana ake aamuna awiri, Manase ndi Efuremu, apite naye.


Ndiponso akapolo a mfumu anadzadalitsa Davide mbuye wathu mfumu, nati, Mulungu wanu aposetse dzina la Solomoni lipunde dzina lanu, nakulitse mpando wake wachifumu upose mpando wanu wachifumu; ndipo mfumu anawerama pakamapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa