Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 11:22 - Buku Lopatulika

22 Ndi chikhulupiriro, Yosefe, pakumwalira, anatchula za matulukidwe a ana a Israele; nalamulira za mafupa ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndi chikhulupiriro, Yosefe, pakumwalira, anatchula za matulukidwe a ana a Israele; nalamula za mafupa ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Pokhala ndi chikhulupiriro, Yosefe ali pafupi kutsirizika, adanenapo za kutuluka kwa Aisraele mu Ejipito, naŵauziratu za m'mene adaayenera kudzachitira ndi mafupa ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Ndi chikhulupiriro Yosefe ali pafupi kumwalira anayankhula za kutuluka kwa Aisraeli mu Igupto ndipo anawawuza zoti adzachite ndi mafupa ake.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:22
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anamuka nao mafupa a Yosefe; pakuti adawalumbiritsatu ana a Israele ndi kuti, Mulungu adzakuzondani ndithu ndipo mukakwere nao mafupa anga osawasiya kuno.


amene anaonekera mu ulemerero, nanena za kumuka kwake kumene Iye ati adzatsiriza ku Yerusalemu.


ndipo anawanyamula kupita nao ku Sekemu, nawaika m'manda amene Abrahamu adagula ndi mtengo wake wa ndalama kwa ana a Hamori mu Sekemu.


Ndipo mafupa a Yosefe amene ana a Israele anakwera nao kuchokera ku Ejipito anawaika ku Sekemu, pa kadziko kamene adakagula Yakobo kwa ana a Hamori atate wa Sekemu ndi kuwapatsa ndalama zana; ndipo anakhala cholowa cha ana a Yosefe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa