Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 11:20 - Buku Lopatulika

20 Ndi chikhulupiriro Isaki anadalitsa Yakobo ndi Esau, zingakhale za zinthu zilinkudza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndi chikhulupiriro Isaki anadalitsa Yakobo ndi Esau, zingakhale za zinthu zilinkudza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Pokhala ndi chikhulupiriro, Isaki adapemphera ana ake, Yakobe ndi Esau, madalitso am'tsogolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ndi chikhulupiriro Isake anadalitsa Yakobo ndi Esau pa zatsogolo lawo.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:20
3 Mawu Ofanana  

nundikonzere ine chakudya chokolera chonga chomwe ndichikonda ine, nudze nacho kwa ine kuti ndidzadye; kuti moyo wanga ukadalitse iwe ndisanafe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa