Ahebri 11:10 - Buku Lopatulika10 pakuti analindirira mzinda wokhala nao maziko, mmisiri wake ndi womanga wake ndiye Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 pakuti analindirira mudzi wokhala nao maziko, mmisiri wake ndi womanga wake ndiye Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Monsemo Abrahamu ankadikira mzinda wa maziko okhazikika. Mzindawo, Mmisiri woganiziratu mamangidwe ake ndiponso woumanga, ndi Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti amadikira mudzi wokhala ndi maziko, umene mmisiri ndi womanga wake ndi Mulungu. Onani mutuwo |