Ahebri 10:5 - Buku Lopatulika5 Mwa ichi polowa m'dziko lapansi, anena, Nsembe ndi chopereka simunazifune, koma thupi munandikonzera Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwa ichi polowa m'dziko lapansi, anena, Nsembe ndi chopereka simunazifuna, koma thupi munandikonzera Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nchifukwa chake pamene Khristu adadza pansi pano, adati, “Inu Mulungu simudafune nsembe kapena zopereka, koma thupi mudandikonzera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Nʼchifukwa chake Khristu atabwera pa dziko lapansi anati, “Simunafune nsembe kapena zopereka, koma thupi munandikonzera. Onani mutuwo |