Ahebri 10:26 - Buku Lopatulika26 Pakuti tikachimwa ife eni ake, titatha kulandira chidziwitso cha choonadi, siitsalanso nsembe ya kwa machimo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pakuti tikachimwa ife eni ake, titatha kulandira chidziwitso cha choonadi, siitsalanso nsembe ya kwa machimo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Pakuti tikamachimwirachimwira mwadala, kwina tikudziŵa choona, palibenso nsembe ina iliyonse ingaperekedwe chifukwa cha machimo athuwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ngati ife tipitirira kuchimwa mwadala pamene tikudziwa choona, palibenso nsembe ina imene ingaperekedwe chifukwa cha machimo athuwo. Onani mutuwo |