Ahebri 10:27 - Buku Lopatulika27 koma kulindira kwina koopsa kwa chiweruziro, ndi kutentha kwake kwa moto wakuononga otsutsana nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 koma kulindira kwina koopsa kwa chiweruziro, ndi kutentha kwake kwa moto wakuononga otsutsana nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pamenepo chotitsalira si china ai, koma kumangodikira ndi mantha chiweruzo, ndiponso moto woopsa umene udzaononga otsutsana ndi Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Koma kumangodikira kokha ndi mantha chiweruzo ndiponso moto woopsa umene udzawononga adani a Mulungu Onani mutuwo |