Ahebri 10:25 - Buku Lopatulika25 osaleka kusonkhana kwathu pamodzi, monga amachita ena, komatu tidandaulirane, ndiko koposa monga momwe muona tsiku lilikuyandika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 osaleka kusonkhana kwathu pamodzi, monga amachita ena, komatu tidandaulirane, ndiko koposa monga momwe muona tsiku lilikuyandika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Tisamakhalakhala ku misonkhano yathu, monga adazoloŵera ena, koma ife tizilimbitsana mtima, makamaka poona kuti tsiku la Ambuye likuyandikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Tiyeni tisaleke kusonkhana kwathu pamodzi monga mmene ena amachitira, koma tizilimbikitsana makamaka poona kuti tsiku la Ambuye layandikira. Onani mutuwo |