Ahebri 10:24 - Buku Lopatulika24 ndipo tiganizirane wina ndi mnzake kuti tifulumizane ku chikondano ndi ntchito zabwino, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndipo tiganizirane wina ndi mnzake kuti tifulumizane ku chikondano ndi ntchito zabwino, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tizikumbukirana kuti tilimbikitsane kukondana ndi kuchita ntchito zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Tiziganizira mmene tingalimbikitsirane wina ndi mnzake pokondana ndi kuchita ntchito zabwino. Onani mutuwo |