Ahebri 10:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo pokhala nacho, abale, chilimbikitso chakulowa m'malo opatulika, ndi mwazi wa Yesu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo pokhala nacho, abale, chilimbikitso chakulowa m'malo opatulika, ndi mwazi wa Yesu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Motero tsono, abale, timayembekeza mosakayika konse kuloŵa m'Malo Opatulika Kopambana chifukwa cha imfa ya Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo tsono abale, molimba mtima timalowa mʼMalo Opatulika kwambiri chifukwa cha magazi a Yesu. Onani mutuwo |