Ahebri 10:20 - Buku Lopatulika20 pa njira yatsopano ndi yamoyo, imene adatikonzera, mwa chotchinga, ndicho thupi lake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 pa njira yatsopano ndi yamoyo, imene adatikonzera, mwa chotchinga, ndicho thupi lake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Iye adatitsekulira njira yatsopano ndi yamoyo yobzola chochinga, chimene chili thupi lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anatitsekulira njira yatsopano ndi yamoyo kudutsa chinsalu chotchinga, chimene ndi thupi lake. Onani mutuwo |