Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 10:18 - Buku Lopatulika

18 Koma pomwe pali chikhululukiro cha machimo palibenso chopereka cha kwa uchimo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Koma pomwe pali chikhululukiro cha machimo palibenso chopereka cha kwa uchimo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pamene Mulungu wakhululukira zonsezi, sipafunikanso nsembe yoperekera machimo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo pamene machimo akhululukidwa, sipafunikanso nsembe yoperekedwa chifukwa cha machimowo.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 10:18
4 Mawu Ofanana  

Pakuti ndi chipereko chimodzi anawayesera angwiro chikhalire iwo oyeretsedwa.


ndipo machimo ao ndi kusaweruzika kwao sindidzakumbukiranso.


Ndipo pokhala nacho, abale, chilimbikitso chakulowa m'malo opatulika, ndi mwazi wa Yesu,


Pakadapanda kutero, kodi sakadaleka kuzipereka, chifukwa otumikirawo sakadakhala nacho chikumbumtima cha machimo, popeza adayeretsedwa kamodzi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa