Ahebri 10:17 - Buku Lopatulika17 ndipo machimo ao ndi kusaweruzika kwao sindidzakumbukiranso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 ndipo machimo ao ndi masaweruziko ao sindidzawakumbukiranso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pambuyo pake akutinso, “Sindidzaŵakumbukiranso konse machimo ao ndi zolakwa zao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndipo akutinso: “Sindidzakumbukiranso konse machimo awo ndi zolakwa zawo.” Onani mutuwo |