Ahebri 1:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo pamene atenganso wobadwa woyamba kulowa naye m'dziko, anena, Ndipo amgwadire Iye angelo onse a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo pamene atenganso wobadwa woyamba kulowa naye m'dziko, anena, Ndipo amgwadire Iye angelo onse a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma pamene ankatuma Mwana wake wachisamba pansi pano, Mulungu adati, “Angelo onse a Mulungu azimpembedza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene Mulungu amatuma Mwana wake woyamba kubadwa ku dziko lapansi anati, “Angelo onse a Mulungu amupembedze Iye.” Onani mutuwo |