Ahebri 1:14 - Buku Lopatulika14 Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Nanga angelo, kodi suja iwo ndi mizimu yotumikira chabe, imene Mulungu amaituma chifukwa cha anthu odzalandira chipulumutso? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kodi angelo onse si mizimu yotumikira odzalandira chipulumutso? Onani mutuwo |