Ahebri 1:13 - Buku Lopatulika13 Koma za mngelo uti anati nthawi iliyonse, Khala padzanja lamanja langa, Kufikira ndikaika adani ako mpando wa kumapazi ako? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma za mngelo uti anati nthawi iliyonse, Khala pa dzanja lamanja langa, Kufikira ndikaika adani ako mpando wa kumapazi ako? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nkale lonse Mulungu sadauzepo mngelo aliyense kuti, “Khala ku dzanja langa lamanja mpaka ndisandutse adani ako kuti akhale ngati chopondapo mapazi ako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kodi ndi kwa Mngelo uti kumene Mulungu ananenapo kuti, “Khala kudzanja langa lamanja mpaka nditapanga adani ako kukhale chopondapo mapazi ako.” Onani mutuwo |