Afilipi 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ichi ndipempha, kuti chikondi chanu chisefukire chionjezere, m'chidziwitso, ndi kuzindikira konse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ichi ndipempha, kuti chikondi chanu chisefukire chionjezere, m'chidziwitso, ndi kuzindikira konse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chinke chikukulirakulira pamodzi ndi nzeru ndi kumvetsetsa zinthu mozama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chipitirire kukulirakulira pa chidziwitso ndi kuzama mʼmaganizo, Onani mutuwo |