Afilipi 1:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chipitirire kukulirakulira pa chidziwitso ndi kuzama mʼmaganizo, Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Ndipo ichi ndipempha, kuti chikondi chanu chisefukire chionjezere, m'chidziwitso, ndi kuzindikira konse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ichi ndipempha, kuti chikondi chanu chisefukire chionjezere, m'chidziwitso, ndi kuzindikira konse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chinke chikukulirakulira pamodzi ndi nzeru ndi kumvetsetsa zinthu mozama. Onani mutuwo |