Afilipi 1:17 - Buku Lopatulika17 koma ena alalikira Khristu mochokera m'chotetana, kosati koona, akuyesa kuti adzandibukitsira chisautso m'zomangira zanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 koma ena alalikira Khristu mochokera m'chotetana, kosati koona, akuyesa kuti adzandibukitsira chisautso m'zomangira zanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma oyamba aja salalika Khristu moona. Amangodzikonda okha, ndipo amafuna kundiwonjezera zoŵaŵa pamene ndili m'ndende muno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ena aja amalalikira Khristu modzikonda osati moona mtima namaganiza kuti kutero kubweretsa mavuto pamene ndili mʼmaunyolo. Onani mutuwo |