Afilipi 1:15 - Buku Lopatulika15 Enatu alalikiranso Khristu chifukwa cha kaduka ndi ndeu; koma enanso chifukwa cha kukoma mtima; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Enatu alalikiranso Khristu chifukwa cha kaduka ndi ndeu; koma enanso chifukwa cha kukoma mtima; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Alipodi ena amene amalalika Khristu chifukwa cha kaduka ndi kukonda mikangano. Koma aliponso ena amene amamlalika ndi mtima woona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Nʼzoonadi kuti ena amalalikira Khristu chifukwa cha kaduka ndi mikangano, koma ena chifukwa cha zolinga zabwino. Onani mutuwo |