Afilipi 1:12 - Buku Lopatulika12 Koma abale, ndifuna kuti muzindikire kuti zija za kwa ine zidachita makamaka kuthandizira Uthenga Wabwino; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma abale, ndifuna kuti muzindikire kuti zija za kwa ine zidachita makamaka kuthandizira Uthenga Wabwino; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Abale, ndikufuna kuti mudziŵe kuti zimene zandigwera, zathandiza ndithu kufalitsa Uthenga Wabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti chimene chandichitikira ine chathandiza kwambiri kupititsa patsogolo Uthenga Wabwino. Onani mutuwo |