Afilipi 1:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsopano abale, ndikufuna mudziwe kuti chimene chandichitikira ine chathandiza kwambiri kupititsa patsogolo Uthenga Wabwino. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Koma abale, ndifuna kuti muzindikire kuti zija za kwa ine zidachita makamaka kuthandizira Uthenga Wabwino; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma abale, ndifuna kuti muzindikire kuti zija za kwa ine zidachita makamaka kuthandizira Uthenga Wabwino; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Abale, ndikufuna kuti mudziŵe kuti zimene zandigwera, zathandiza ndithu kufalitsa Uthenga Wabwino. Onani mutuwo |