Aefeso 6:11 - Buku Lopatulika11 Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Valani zida zonse zimene Mulungu akupatsani, kuti muthe kulimbika polimbana ndi ndale za Satana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Valani zida zonse za Mulungu kuti muthe kuyima ndi kukana machenjerero a Satana. Onani mutuwo |