Aefeso 6:10 - Buku Lopatulika10 Chotsalira, tadzilimbikani mwa Ambuye, ndi m'kulimba kwa mphamvu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chotsalira, tadzilimbikani mwa Ambuye, ndi m'kulimba kwa mphamvu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Potsiriza ndikuti, dzilimbitseni mwa Ambuye, mwa mphamvu yao yaikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Potsiriza ndikuti, dzilimbitseni mwa Ambuye ndi mwa mphamvu zake zazikulu. Onani mutuwo |