Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 5:30 - Buku Lopatulika

30 pakuti tili ziwalo za thupi lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 pakuti tili ziwalo za thupi lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Amatero chifukwa Mpingowo ndi thupi lake, ndipo ife ndife ziwalo zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 pakuti ndife ziwalo za thupi lake.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 5:30
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.


chomwecho ife, ndife ambiri, tili thupi limodzi mwa Khristu, ndi ziwalo zinzake, wina ndi wina.


Kodi simudziwa kuti matupi anu ali ziwalo za Khristu? Chifukwa chake ndidzatenga ziwalo za Khristu kodi, ndi kuziyesa ziwalo za mkazi wachiwerewere? Msatero iai.


amene ali thupi lake, mdzazidwe wa Iye amene adzaza zonse m'zonse.


pakuti munthu sanadane nalo thupi lake ndi kale lonse; komatu alilera nalisunga, monganso Khristu Mpingo;


kuchokera kwa Iye amene thupi lonse, lothandizidwa ndi kulumikizidwa pamodzi mwa mfundo ndi mitsempha, likula ndi makulidwe a Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa