Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Aefeso 5:31 - Buku Lopatulika

31 Chifukwa cha ichi munthu azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wake; ndipo iwo awiri adzakhala thupi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Chifukwa cha ichi munthu azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wake; ndipo iwo awiri adzakhala thupi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Paja mau a Mulungu akuti, “Nchifukwa chake mwamuna adzasiye atate ndi amai ake, nkukaphatikizana ndi mkazi wake, kuti aŵiriwo asanduke thupi limodzi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 “Pa chifukwa ichi, mwamuna adzasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi.”

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 5:31
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.


nati, Chifukwa cha ichi mwamuna adzasiya atate wake ndi amake, nadzaphatikizana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi?


Kapena simudziwa kuti iye wophatikidwa ndi mkazi wachiwerewere ali thupi limodzi? Pakuti awiriwo, ati, adzakhala thupi limodzi.


Chinsinsi ichi nchachikulu; koma ndinena ine za Khristu ndi Mpingo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa