Aefeso 5:29 - Buku Lopatulika29 pakuti munthu sanadane nalo thupi lake ndi kale lonse; komatu alilera nalisunga, monganso Khristu Mpingo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 pakuti munthu sanadana nalo thupi lake ndi kale lonse; komatu alilera nalisunga, monganso Khristu Mpingo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Palibiretu munthu amene amadana ndi thupi lake, koma amalidyetsa ndi kulisamala bwino, monga momwe Khristu amachitira Mpingo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Pakuti palibe amene amadana nalo thupi lake, koma amalidyetsa ndi kulisamalira bwino, monga momwe Khristu amachitira ndi mpingo wake Onani mutuwo |