Aefeso 5:14 - Buku Lopatulika14 Mwa ichi anena, Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndipo Khristu adzawala pa iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mwa ichi anena, Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndipo Khristu adzawala pa iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Motero chilichonse choonekera poyera, chimasanduka kuŵala. Nchifukwa chake amati, “Dzuka wam'tulo iwe, uka kwa akufa, ndipo Khristu adzakuŵalira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Nʼchifukwa chake Malemba akuti, “Dzuka, wamtulo iwe, uka kwa akufa, ndipo Khristu adzakuwalira.” Onani mutuwo |