Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 5:13 - Buku Lopatulika

13 Koma zinthu zonse potsutsika ndi kuunika, zionekera; pakuti chonse chakuonetsa chili kuunika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Koma zinthu zonse potsutsika ndi kuunika, zionekera; pakuti chonse chakuonetsa chili kuunika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Koma kuŵala kumaunika zinthu, ndipo zonse zimaonekera poyera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Koma kuwala kumawunikira zinthu, ndipo chilichonse chimaonekera poyera. Choncho chilichonse choonekera poyera chimasandukanso kuwala.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 5:13
8 Mawu Ofanana  

Aneneri ako anakuonera masomphenya achabe ndi opusa; osawulula mphulupulu yako kuti abweze undende wako, koma anakuonera manenero achabe ndi opambutsa.


Ndipo tsopano ndidzaonetsa manyazi ake pamaso pa omkonda, popandanso wakumlanditsa m'dzanja langa.


M'mene ndichiritsa Israele, mphulupulu ya Efuremu ivumbuluka, ndi zoipa za Samariya; pakuti achita bodza, ndipo mkhungu alowa m'nyumba, ndi gulu la mbala lilanda kubwalo.


Ndidzasenza mkwiyo wa Yehova, chifukwa ndamchimwira, mpaka andinenera mlandu wanga, ndi kundiweruzira mlandu wanga; adzanditulutsira kwa kuunika, ndipo ndidzapenya chilungamo chake.


Chifukwa chake musaweruze kanthu isanadze nthawi yake, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wake wa kwa Mulungu.


pakuti zochitidwa nao m'tseri, kungakhale kuzinena kuchititsa manyazi.


Koma za mngelo uti anati nthawi iliyonse, Khala padzanja lamanja langa, Kufikira ndikaika adani ako mpando wa kumapazi ako?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa