Aefeso 5:13 - Buku Lopatulika13 Koma zinthu zonse potsutsika ndi kuunika, zionekera; pakuti chonse chakuonetsa chili kuunika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma zinthu zonse potsutsika ndi kuunika, zionekera; pakuti chonse chakuonetsa chili kuunika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma kuŵala kumaunika zinthu, ndipo zonse zimaonekera poyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma kuwala kumawunikira zinthu, ndipo chilichonse chimaonekera poyera. Choncho chilichonse choonekera poyera chimasandukanso kuwala. Onani mutuwo |