Aefeso 5:12 - Buku Lopatulika12 pakuti zochitidwa nao m'tseri, kungakhale kuzinena kuchititsa manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 pakuti zochitidwa nao m'tseri, kungakhale kuzinena kuchititsa manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Paja zimene iwo amachita mobisa, ngakhale kuzitchula komwe kumachititsa manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pakuti ndi zochititsa manyazi ngakhale kutchula zomwe zimachitika mseri. Onani mutuwo |